nya-x-nyanja_luk_text_reg/05/33.txt

1 line
417 B
Plaintext

\v 33 \v 34 \v 35 Ananena kwaiye, ''Kuti ophunzila ba Yoani bamakonda kupempela ndi kusala kudya kambiri, ndiponso ophunzila abafalisi bachitachimozimozi.Koma afalisi bako bakudya na kumwa.'' Yesu ananena kwaiwo, '' Kodi munthu angapange ukwati wa banthubake bamukwati nakubaleka kutibasale kudya, pamene mukwati akalinabo? Koma masiku yazabwela pamene mukwati azatengewa kwaiyo, Ndiponso masiku yaja bangasale kudya.