nya-x-nyanja_luk_text_reg/05/25.txt

1 line
271 B
Plaintext

\v 25 \v 26 Pamene apo anapita kuntangu kwao na kunyamula mpasa yamene analikugonapo. Ndiponso anabwelelamo kunyumba kwao, ndikutamanda Mulungu. Alionse anadabwa ndiponso banalemekeza Mulungu. Banazozedwa ndi kuyopa, nakunena, ''Kuti taona zinthu zamene zopambana lelo.''