nya-x-nyanja_luk_text_reg/05/17.txt

1 line
321 B
Plaintext

\v 17 Chinabwela chachitika chakuti, muyaja masiku yamene analikupunzisa, Ndiponso kunali afalisi ndi apunzisi amalamulo analichinkhalile kwamenekuja amene anabwela kumalo yambiri yaminzi zosiyana muzigao zija za muGalileyo ndiponso mu Judeya, ndiponso mumunzi wamu Jelusalemu.Mphamvu za Mulungu zochilisa zinali paliiye.