nya-x-nyanja_luk_text_reg/05/08.txt

1 line
547 B
Plaintext

\v 8 \v 9 \v 10 \v 11 Simoni Petulo, pamene anaona ichi, anagwela pansi pamapazi ya Yesu, ndikunena, '' Chokani paliine, chifukwa ndine munthu ochimwa, Ambuye.'' Chifukwa chinamudabwisa, ndiponso ndi iwobameneanalinabo, pakugwila kwansomba zamene banatenga. Aba banali kuikilako Yakob ndiponso Yoani, mwana mwamuna wa Zebedi, bamenebanali kugwilizana nabopamozi ndi Simoni. Ndiponso Yesu ananena kuli Simoni, '' Usayope, chikukwa kuchokela manje uzayamba kugwila banthu.'' Pamene banaleta zongwililalo nsomba kunthaka, banasiya zonse ndikumukonka.