nya-x-nyanja_luk_text_reg/05/04.txt

1 line
584 B
Plaintext

\v 4 \v 5 \v 6 \v 7 Pamene anasiliza kukamba, Ananena kuli Simoni, '' Tenga boti ndiponso uipeleka pamanzi yamene yalimumalo mombila maningi pakuti mugwile.'' Simoni anayankha ndikunena kuti, ''Mfumu, tasebenza usiku onse, ndiponso sitinagwilepo kalikonse, koma kamba kamau yanu, nizangenesa zogwililamo nsomba pamanzi yombila.'' Pamene bana chita izi, bana unjika nsomba zambiri, ndiponso zogwililamo zao zinali kung'ambika.Koma banaenda kulibanzao bamene banali muboti inangu kuti babwele babatandizile.Banabwela ndiponso bana zuzha maboti yonse yabili, chakuti yanayamba nakumbila.