nya-x-nyanja_luk_text_reg/06/20.txt

1 line
244 B
Plaintext

\v 20 \v 21 Ndiponso anayanganila paophunzila bake, ndi kunene, ''Ndimwe odala imweamene aliosauka, chifukwa ufumu wa Mulungu ndiye wanu. Ndimwe odala bamene mulinanjala, chifukwa muzazozedwa. Ndimwe odala imwe bamene mulila, chifukwa muzaseka.