nya-x-nyanja_luk_text_reg/01/18.txt

1 line
495 B
Plaintext

\v 18 \v 19 \v 20 Zakaliya ananena kwamungelo, '' kuti ningazibe bwanji izi? popeza ndine mwamuna okakalamba ndi mukazi wanga niokotata maningi.'' mungelo anayankha ndi kunena kuli iye, ''Ndine Gabuliyela, wamene aimilila mumanso pa Mulungu. nenze ninatumiwa kukamba naimwe, kuleta uyu utenga wabwino.Ndiponso, uzankhala chete, ndikukangiwa kukamba, kufikila na siku lamene izi zinthu zi zafikilizika.Ichi nichifukwa chakuti siunakululupile mau yanga, yamene yazafikilizika pa nthawi yokwana.''