nya-x-nyanja_luk_text_reg/01/42.txt

1 line
445 B
Plaintext

\v 42 \v 43 \v 44 \v 45 Ananyamula ndi liu lake na kukambila pamwamba, Odala ndinu pabakazi, ndiponso zibeleko za mumimba mwanu nizodala.Ndiponso nichifukwa chachani kuti chachitika kwaine kuti amai ba Mulungu wanga kuti angabwele kwaine? Koma onani, pamene liu lakuposha kwanu labwela kumatu yanga, mwana mumimba yanga ajumpa na chimwemwe.Ndiponso niodala wamene akulupilila chifukwa kuzankhala kufilizika kwamau yamene Mulungu anena kwa iye.''