nya-x-nyanja_luk_text_reg/01/39.txt

1 line
331 B
Plaintext

\v 39 \v 40 \v 41 Koma mariya pamasiku yaja anaima mwamusanga ndiponso anenda muziko lamaphiri, mumuzinda wa judeya. Anaenda munyumba ya Zachariya ndi kuposhana na Elizabeta.Koma chinachitika nichakuti pamene Elizabeta anamvela moni wa Mariya, mwana mumimba yake anajumpa, ndiponso Elizabeta anazozedwa ndi mphamvu za Muzimu Oyela.