nya-x-nyanja_luk_text_reg/01/21.txt

1 line
365 B
Plaintext

\v 21 \v 22 \v 23 Koma banthu banali kuembekeza Zakaliya. Anali odabwa popeza kuti analikutaya nthawi yambiri mutempele.Ndiponso pamene anachoka, sianakambe ndi bemve. Anazindikila kuti anaona mansompenya pamene anali mutempele.Anapitiliza kualangiza ziziwiso, ndi kunkhala mwakachete.Inabwela yafika nthawi yake yamasiku yosebenza yanasila, Anaenda kunyumba kwake.