nya-x-nyanja_luk_text_reg/07/18.txt

1 line
371 B
Plaintext

\v 18 \v 19 \v 20 Aphunzila ba Yoani anamuuza palizonse izi.Ndiponso Yoani anaitana ophunzila bake babili ndikubatuma kwa ambuye ndikunena, '' Kodi ndimwe amene mufunika kubwela, olo tiyangani kuli winangu?'' Pamene bana bwela pafupi ndi Yesu, Azimuna ananena, '' Kuti Yoani mubadizi atituma kwaiwe ndikunena, ' Kuti kodi ndiwe wamene azabwela, olo tiyanganile winangu?''