nya-x-nyanja_luk_text_reg/07/06.txt

1 line
584 B
Plaintext

\v 6 \v 7 \v 8 Pokapo Yesu anapitiliza munjila yake ndibemve.Koma pamene akalibe kufika patali nanyumba, Uja musenchulyoni anatuma banzake kuli iye, '' Ambuye, musazivutise, chifukwa inesindine oyenela kuti mubwele munyumba yanga. Kamba kachamene ichi sininazione kuti ndine oyenela kuti mubwele kwaine, Koma kamabani chabemau ndiponso wanchinto wanga azapola. chifukwa naine ndine munthu wamene alamulila asilikale. Nimane kuli uyu, 'kuti enda', ndiponso ayenda, ndiponso amanena kuli wina, ' bwela, 'ndiponso abwela, ndiponso kuli wanchito wanga, ' chita ichi, 'ndiponso amachita,''