nya-x-nyanja_luk_text_reg/06/39.txt

1 line
285 B
Plaintext

\v 39 \v 40 Ndiponso anabauza nthano, ''Kodi nanga munthu osaona angasogolele muzake wamene siaona? ngati angachiti, Ndiponso bonse bazagwela mumugodi, kodi simwamene?'' Ophunzila simukulu kupambana muphunzisi, koma alionse ngati afikapo pakuphunzisiwa azanhkala monga muphunzisi wake.