nya-x-nyanja_luk_text_reg/06/35.txt

1 line
342 B
Plaintext

\v 35 \v 36 Koma kondani adani banu ndiponso bachitileni vabwino.Kongolesani koma musaganizile kulandila chilichonse ndiponso mphatso yanu izankhala yaikulu ndiponso muzankhala bana babapamwamba, chifukwa iye mwinewake niwabwino kulibaja banthu bamene sibayamika ndiponso kuli boipa. Nkalani bachifundo, monga mwamene tatewanu ali wachifundo.