nya-x-nyanja_luk_text_reg/06/29.txt

1 line
238 B
Plaintext

\v 29 \v 30 Kuli iwo bamene bakumenyani kutobo, mupasenso ndi kwinakwache.Ngati munthu wina atenga koti yako, usagwilililenso chovala chako. Pasa aliyense wamene akupempa.Ngati munthu wina atenga chinthu chako, usamufunse kuti akubwezele.