nya-x-nyanja_luk_text_reg/06/09.txt

1 line
401 B
Plaintext

\v 9 \v 10 \v 11 Yesu ananena kwaiwo, ''Nikufunsa iwe, Kodi sicholamulidwa pasabata kuchita zabwino kuchila kuchita voipa, kupulumusa moyo kuchila kuuononga?'' Ndiponso anayanga baja bonse banamuzungulila ndikunena ku mwamuna, ''Tambusula kwanja yako.'' Anachita chomwecho, ndiponso kwanja kwake kunabwezewa. Ndiponso banazozedwa naukali ndiponso ananena kuliwina ndi muzaka chamene bangamuchite Yesu.