nya-x-nyanja_luk_text_reg/03/01.txt

1 line
411 B
Plaintext

\c 3 \v 1 \v 2 Muchaka chakumi ndi tusanu pamene analikulamulila Tibarias siza_ pamene ponshas paileti anali mukulu wa boma mu judeya, Helodi anali tetrachi wamu galili, mubale wake philipu anali tetrachi muchigao cha ituriya ndiponso trachonitis, ndiponso lysanias anali tetrachi wa Abileni, ija nthawi ya opelekanse ya Annas ndiponso kefasi_ mau ya Mulungu wanabwela kuli Yoani mwana wa Zakaliya, muchipululu.