nya-x-nyanja_luk_text_reg/02/39.txt

1 line
259 B
Plaintext

\v 39 \v 40 Pamene anasiliza zonse izi banali kufunikila kuchita kulingani ndi malamulo ya Mulungu, Banabwelela kugalileyo, mumuzinda wao wa Nazareti. Mwana anakula ndiponso anali ndi mphamvu, kuchulukila munzelu ndiponso chisomo cha Mulungu chinali pali iye.