nya-x-nyanja_luk_text_reg/02/33.txt

1 line
401 B
Plaintext

\v 33 \v 34 \v 35 Batate ba mwana na bamai bake anali odabwisiwa panzithu zamene zina kambika pali iye. Simoni anaba dalitsa ndi kune kwa kuli Maliya mai wake, '' Onani, uyu mwana anasankidwa kwaio bamene ogwesewa ndi kunyamuliwa kwa banthu bambili mu Izilaeli ndiponso kwachiziwiso chamene chinakaniwa__ ndiponso monga lupanga ong'amba umoyo wanu_ pakuti maganizilo yamitima zambili ya vumbulusiwe.''