nya-x-nyanja_luk_text_reg/02/25.txt

1 line
280 B
Plaintext

\v 25 \v 26 Kunaliko mwamuna mujelusalemu otanidwa simoni ndiponso anali olungama ndi ozipelaka.Anali kuyanganila pakubwezewa kwa Izilaeli,Ndiponso muzimu oyela anali paliiye.Chenze chinavumbulusiwa kwaiye na muzimu oyela kuti siazaona infa pamene akalibe kuona ambuye wa kristhu.