nya-x-nyanja_luk_text_reg/02/04.txt

1 line
299 B
Plaintext

\v 4 \v 5 Ndi Yosefe anapita kuchokela kugalileyo,mumuzinda wa nazareti, nakuyenda ku judeya, mumuzinda wamene uitanidwa Davidi wamu betilehemu, chifukwa analikuchokela mubanja ya mubado wa Davidi.Anapita kuja kukalembesa pamozi ndi Mariya, wamene enze okolobekelewa kuli iye ndiponso anali namimba.