\v 12 \v 13 Chinabwela chachitika masiku yaja nichakuti anaenda kuluphiri kupempela. Anapitiliza kupempela kwa Mulungu usiku onse. Pamene kunali muzuba, anaitana opunzila bake, ndiponso anasankha kumi ndi tuwili bamene analikuitana ati maapostoli.