nya-x-nyanja_jud_text_reg/01/22.txt

1 line
189 B
Plaintext

\v 22 Nkalani na chifundo kwaibo bamene sibanakhulupirile. Pulumusani bena ndikubachosa mumulilo. \v 23 Kuli bena munkhale ba chifundo ndi kuyopa. Muzondenso na zovala zotimbiridwa za tupi.