nya-x-nyanja_jud_text_reg/01/17.txt

1 line
307 B
Plaintext

\v 17 Koma, inu bokondedwa, kumbukani mau yamene Ambuye Yesu Kristu anakamba ku mbuyo uku kupitila mu atumwi. \v 18 Banakamba kwainu ati, "Mu ntawi yo tera kuzankala banthu boseka chikulupiliro bamene bazakonka zifunilo zawo za uchimo." \v 19 Aba banthu nibopatukisa. Bakonda za muziko, ndipo balibe Muzimu.