nya-x-nyanja_jud_text_reg/01/14.txt

1 line
521 B
Plaintext

\v 14 Enocki, wa nambala seveni kuchoka pa Adam, anapa uneneri pali beve ati, "Onani! Ambuye abwera ndi banthu bambiri makaana na makaana nabo yela bake. \v 15 Abwera kupasa chiwerudzo pamunthu onse. Abwera kugojensa bonse bamene bachita nchito zoyipa zamene bachitila mukuyipa kwao, ndipo na mau onse ya ntota yamene aba ba machimo banakamba kwa iye. \v 16 Aba bang'ung'uza, ba madandaulo, bamene bakonka zifunilo zao za uchimo. Ndipo ni bozinvela, bamene pakuti vintu vibayendele mushe bekabeka, bama tilimula ba nzao.