nya-x-nyanja_jud_text_reg/01/12.txt

1 line
391 B
Plaintext

\v 12 Aba ndiye bamene bazibisa mumagulu ya ma pwando yachikunja. Ba ma kondyelela kopanda nsoni, bangozidwesa bene beka. Nimakumbi yalimbe manzi, otengewa chabe na mpepo. Ni mitengo zamu ntawi yo panda mvula zilibe vipaso - bokufa kabili, bong'ámbika na mizu. \v 13 Ndi mafuunde oyipa pa chimana, bopanga manyazi yabo. Ni nyenyezi zosokera, zimene mudima wakuda unusungiwa masiku osasila.