nya-x-nyanja_jud_text_reg/01/09.txt

1 line
493 B
Plaintext

\v 9 Koma na Mikayeli mukulu wa angelo, pamene enze kusushanya na Satana pa tupi ya Mose sana yese kumuuza choyipa yayi. Koma anamuuza kuti, "Ambuye akuzuzule!" \v 10 Koma aba bantu ba makamba vo kambakamba pa zitu zilizonse zamene sibaziba mushe. Ndipo baziba chabe - monga vinyama vosaganiza viziba muchizibiso - ivi ndiye vinabaononga. \v 11 Soka kwa eve! Chifukwa banayenda njila ya Kaini, ndipo banizingenesa muku lakwa kwa Balaamu kofuna kudyelamo. Banaonongekela mu kupanduka kwa Korah.