Fri Nov 09 2018 14:02:35 GMT+0200 (South Africa Standard Time)

This commit is contained in:
tsDesktop 2018-11-09 14:02:35 +02:00
parent b5ebf2b19a
commit a8a7019ca7
2 changed files with 2 additions and 2 deletions

View File

@ -1 +1 @@
\v 14 Ndipo Enocki, wa nambala seveni kuchoka pa Adam, anapa uneneri pali beve ati, "Onani! Ambuye abwera ndi banthu bambiri makaana na makaana babo yela bake. \v 15 Abwera kupasa chiwerudzo pamunthu onse. Abwera kugojensa bonse bamene bachita nchito zoyipa zamene bachitila mukuyipa kwao, ndipo nama mau onse ya ntota yamene aba ba machimo banakamba kwa iye. \v 16 Aba ni bung'ung'uza, ba madandaulo, bamene bakonka zifunilo zao za uchimo. Ndipo ni ba vingazi, bamene pakuti vintu vibayendele mushe bekabeka, ba mazitutumula wina ndi muzake.
\v 14 Ndipo Enocki, wa nambala seveni kuchoka pa Adam, anapa uneneri pali beve ati, "Onani! Ambuye abwera ndi banthu bambiri makaana na makaana nabo yela bake. \v 15 Abwera kupasa chiwerudzo pamunthu onse. Abwera kugojensa bonse bamene bachita nchito zoyipa zamene bachitila mukuyipa kwao, ndipo na mau onse ya ntota yamene aba ba machimo banakamba kwa iye. \v 16 Aba ni bung'ung'uza, ba madandaulo, bamene bakonka zifunilo zao za uchimo. Ndipo ni ba vingazi, bamene pakuti vintu vibayendele mushe bekabeka, ba mazitutumula wina ndi muzake.

View File

@ -1 +1 @@
\v 17 Koma, inu bokondewa, kumbukani mau yamene Ambuye Yesu Kristu anakamba ku mbuyo uku kupitila mu ba Mutumika. \v 18 Banakamba kwainu ati, "Mu ntawi yo tera kuzankala banthu otonza bamene bazakonka zifunilo zawo za uchimo." \v 19 Aba banthu nibopatukisa. Bakonda za muziko, ndipo balibe Muzimu.
\v 17 Koma, inu bokondedwa, kumbukani mau yamene Ambuye Yesu Kristu anakamba ku mbuyo uku kupitila mu ba Mutumiki. \v 18 Banakamba kwainu ati, "Mu ntawi yo tera kuzankala banthu otonza bamene bazakonka zifunilo zawo za uchimo." \v 19 Aba banthu nibopatukisa. Bakonda za muziko, ndipo balibe Muzimu.