diff --git a/01/09.txt b/01/09.txt index e28a4fa..d7ed1c4 100644 --- a/01/09.txt +++ b/01/09.txt @@ -1 +1 @@ -\v 9 Koma na Mikayeli mukulu wa angelo, pamene enze kusushanya na Satana pa tupi ya Mose sana yese kumuuza choyipa yayi. Koma anamuuza kuti, "Ambuye akukalipila!" \v 10 Koma aba bantu ba makamba vo kambakamba pa zitu zilizonse zamene sibaziba mushe. Ndipo baziba chabe - vamene ma imbwa osaganiza amaziba kupitila muchibadwire - ivi ndiye vinabaononga. \v 11 Soka kwa eve! Chifukwa banayenda njila ya Kaini, ndipo banizingenesa muku lakwa kwa Balaamu kofuna ndalama. Banaonongekela mu kupanduka kwa Korah. \ No newline at end of file +\v 9 Koma na Mikayeli mukulu wa angelo, pamene enze kusushanya na Satana pa tupi ya Mose sana yese kumuuza choyipa yayi. Koma anamuuza kuti, "Ambuye akuzuzule!" \v 10 Koma aba bantu ba makamba vo kambakamba pa zitu zilizonse zamene sibaziba mushe. Ndipo baziba chabe - vamene ma imbwa osaganiza amaziba kupitila muchibadwire - ivi ndiye vinabaononga. \v 11 Soka kwa eve! Chifukwa banayenda njila ya Kaini, ndipo banizingenesa muku lakwa kwa Balaamu kofuna ndalama. Banaonongekela mu kupanduka kwa Korah. \ No newline at end of file