Fri Nov 09 2018 11:24:38 GMT+0200 (South Africa Standard Time)

This commit is contained in:
tsDesktop 2018-11-09 11:24:38 +02:00
parent 9efaae9dce
commit 580f5817c8
4 changed files with 4 additions and 4 deletions

View File

@ -1 +1 @@
\v 3 \v 4 Bokondedwa, pamene nenze kuyeselela na mphavu zanga zonse kuti ndilembe kwainu pankanni wa chipulumuso chatu tonse, chenzo ufunika kuti nikulimbikiseni kuti muvutikile chi khulupiliro chamene chinapasidwa kwaise na mitima zanu zonse. Chifukwa bantu bena babwela kwainu mukosaziba. Aba bantu banakonzekedwa ku kulangiwa. Ndipo nibantu bochimwa bamene baononga chisomo cha Mulungu watu nochipeleka muuchizende, ndipo bakana Ambuye Mfumu yatu, Yesus Kristu.
\v 3 Bokondedwa, pamene nenze kuyeselela na mphavu zanga zonse kuti ndilembe kwainu pankanni wa chipulumuso chatu tonse, chenzo ufunika kuti nikulimbikiseni kuti muvutikile chi khulupiliro chamene chinapasidwa kwaise na mitima zanu zonse. \v 4 Chifukwa bantu bena babwela kwainu mukosaziba. Aba bantu banakonzekedwa ku kulangiwa. Ndipo nibantu bochimwa bamene baononga chisomo cha Mulungu watu nochipeleka muuchizende, ndipo bakana Ambuye Mfumu yatu, Yesus Kristu.

View File

@ -1 +1 @@
\v 5 \v 6 Apa nifuna kukukumbusani - olo mwenzi ntawi ina mwenze bochiziba chonse - kuti Ambuye anapulumusa bantu ba ku Egipito, koma kuchoka paja anabaononga baja bamene sibanakulupilire. Ndipo bangelo bamene sibanasunge mushe udindo wao wa ulamulilo, koma banasiya mhalo yamene benzofunika kunkhalapo - Mulungu anabamanga mumupata wa muyayaya, muminyololo mo fipa, abasingila siku yoweruuza.
\v 5 Apa nifuna kukukumbusani - olo mwenzi ntawi ina mwenze bochiziba chonse - kuti Ambuye anapulumusa bantu ba ku Egipito, koma kuchoka paja anabaononga baja bamene sibanakulupilire. \v 6 Ndipo bangelo bamene sibanasunge mushe udindo wao wa ulamulilo, koma banasiya mhalo yamene benzofunika kunkhalapo - Mulungu anabamanga mumupata wa muyayaya, muminyololo mo fipa, abasingila siku yoweruuza.

View File

@ -1 +1 @@
\v 7 \v 8 Monga Sodoma na Gommora ndi mizinda nzezo abazunguluka, zinachita vigololo ndiponso zichitwa zina zosayenera kuchitiwa ndi antu. Banabaika chisanzo cha baja bamene banasunzika kuvutika mu moto wosata. Munjila imozi na imozi aba ba maloto ndipo bamaononga ma tupi yabo. Bamakana ulamulilo, ndipo bamakamba zoipa pali abo ba ulemerero.
\v 7 Monga Sodoma na Gommora ndi mizinda nzezo abazunguluka, zinachita vigololo ndiponso zichitwa zina zosayenera kuchitiwa ndi antu. Banabaika chisanzo cha baja bamene banasunzika kuvutika mu moto wosata. \v 8 Manje munjila imozi na imozi aba ba maloto ndipo bamaononga ma tupi yabo. Bamakana ulamulilo, ndipo bamakamba zoipa pali abo ba ulemerero.

View File

@ -1 +1 @@
\v 9 \v 10 \v 11 Koma na Mikayeli mukulu wa angelo, pamene enze kusushanya na Satana pa tupi ya Mose sana yese kumuuza choyipa kwaiye. Koma anamuuza kuti, "Ambuye akukalipila!" Koma aba bantu ba makamba vo kambakamba pa zitu zilizonse zamene sibaziba mushe. Ndipo baziba chabe - vamene ma imbwa osaganiza amaziba kupitila muchibadwire - ivi ndiye vinabaononga. Soka kwa eve! Chifukwa banayenda njila ya Kaini, ndipo banizingenesa muku lakwa kwa Balaamu kofuna ndalama. Banaonongekela mu kupanduka kwa Korah.
\v 9 \v 11 Koma na Mikayeli mukulu wa angelo, pamene enze kusushanya na Satana pa tupi ya Mose sana yese kumuuza choyipa kwaiye. \v 10 Koma anamuuza kuti, "Ambuye akukalipila!" Koma aba bantu ba makamba vo kambakamba pa zitu zilizonse zamene sibaziba mushe. Ndipo baziba chabe - vamene ma imbwa osaganiza amaziba kupitila muchibadwire - ivi ndiye vinabaononga. Soka kwa eve! Chifukwa banayenda njila ya Kaini, ndipo banizingenesa muku lakwa kwa Balaamu kofuna ndalama. Banaonongekela mu kupanduka kwa Korah.