nya-x-nyanja_2jn_text_reg/01/07.txt

1 line
246 B
Plaintext

\v 7 Pakuti bambiri babodza bapita muziko lapansi, ndipo siizindikila kuti Yesus Khristu anabwe mwatupi. uyo ndiye wabodza wosusa Kristu. \v 8 wonesesani pakati panu , kuti musateye zinhtu zamene tasebenzela, koma kuti mukalandile mphaso yokwana.