nya-x-nyanja_2jn_text_reg/01/04.txt

1 line
397 B
Plaintext

\v 4 Nakondwela maningi kupeza bana banu bena bayenda muchoonadi, monga mwamene tinalandilila malamulo kuchokela kuli Mulungu. \v 5 Apa namupapatilani, mukazi - osati monga nilemba malamulo yasopano, koma amozi tilinaye kuchiyambi - kuti tizikondana. \v 6 Ndiponso ichi ndi chikondi, kuti tiziyenda mumalamulo yakhe. Aya ndiye malamulo, monga mwamene munavelela kuchiyambi, ndipo yenda muli ichi.