\v 7 Pakuti bambiri babodza bapita muziko lapansi, ndipo sibazindikila kuti Yesus Kristu anabwela mu tupi. Uyo ndiye wabodza wosusha Kristu. \v 8 Wonesesani pakati panu , kuti musateye zinthu zamene tasebenzela, koma kuti mukalandile mphaso yokwana.