nya-x-nyanja_1pe_text_reg/03/18.txt

1 line
384 B
Plaintext

\v 18 Klistu naye ana vutika chifukwa chama chimo yatu. Eve oyela anatifela, enze oyela, kuti ati bwelese kwa Mulungu. Ana paiwa kumubili koma anauka kumuzimu. \v 19 Mwa muzimu, anapita kulalikila kuba mu ndende. \v 20 Sibana nvelele pamene Mulungu anaba yembekezela mumasiku yanowa. Mumasiku yopanga chi boti na Mulungu ana pulumusa bantu ban'gono-moyo zili chabe 8. kupita mumanzi.