nya-x-nyanja_1pe_text_reg/04/03.txt

1 line
503 B
Plaintext

\v 3 Pakuti ntawi yabwino inapita yamene Mulungu anapasa osa muziba achiti zamene banali kufuna kuti ba chite kukumbwa, kukonda, kukolewa, kukumbwa kumbwa, nakudyela muziko, nakupempela toumba banayamba tosayenela. \v 4 Aba bantu ni bodabwa pamene baona imwe simukanbako voipa vamene bakamba, bama yambakukamba voipa pali imwe. \v 5 Bayembekeze wamene aza weluza bamoyo naba kufa. \v 6 Ndiye chifukwa mau yana lalikiwa kuli bakufa, nangukuti bana ba weluza kumubili, koma bazankala namoyo kumuzimu.