nya-x-nyanja_1pe_text_reg/01/22.txt

1 line
281 B
Plaintext

\v 22 Munapanga moyo yanu bwino pakumvelela chazoona \v 23 .Ichi chinali chachi kondi chapachi bululu,muyenela kukondana kuchokela pansi pamtima.Muna badwa mwa nyowani,osathi nambeu yo onongeka,koma nambeu yamene sionongeka,kupitila mukunkala kwa mau na kusala kwa mau ya mulungu.