nya-x-nyanja_1jn_text_reg/02/20.txt

1 line
225 B
Plaintext

\v 20 Koma mulina muzozo kuchokela kuli oyela.ndiponso bonse muziba choonadi. \v 21 sininalembele kwa imwe chifukwa simunazibe choonadi, koma chifukwa muchiziba ichi ndiponso chifukwa kulibe boza yamene ichokela mu choonadi.