1 line
332 B
Plaintext
1 line
332 B
Plaintext
\v 18 Imwe bana bango'no, iyi ni ntawi yosilizila, monga mwamene munamvelela kuti bambili bosusana kristhu babwela.paichi tiziba kuti ni ntawi yosilizila. \v 19 Banachokela kuliise , koma sibana chokele mwaise. chifukwa ngati banalikuchokela mwaise, asembe anankhalilila mwaise. koma pamene banaenda, sibalangiza kuchokela kuliise. |