1 line
304 B
Plaintext
1 line
304 B
Plaintext
\c 2 \v 1 Imwe bana bango'no, nikulembelani izi zinthu kuti musachimwe.koma ngati wina achimwa, tilinaye otipapatila ndi atata, Yesu Kristhu wamene ali oyela. \v 2 Ni muombolo wama chimo yatu, Ndiponso siise teka, Ndiponso wa ziko lonse. \v 3 Paliichi tiziba kuti timuziba:ngati tasunga malamulo yake. |