nya-x-nyanja_1jn_text_reg/02/04.txt

1 line
352 B
Plaintext

\v 4 Wamene akamba, ''Ati ni muziba Mulungu,'' koma siasunga malamulo yake,ni waboza, na choonadi sichi muli iye. \v 5 koma wamene asunga mau yake,choonadi, ndiye wamane batate ba konda ndi choonadi chake ni chosilizika. paliichi tiziba kuti, timuziba. \v 6 Wamene akamba kuti azankalili muli iye, afunikila kuyenda monga mwame Yesu Kristhu anaendela.