nya-x-nyanja_1jn_text_reg/05/16.txt

1 line
341 B
Plaintext

\v 16 Ngati alionse aona mubale wake achita chimo yamene siipeleka kuimfa, afunika apempele, ndi Mulungu azamupasa umoyo. nikamba oaliaboabo bamene machimo yao siapeleka kuimfa. kuli chimo yamene isanduka ku imfa; sinikamba kuti anga pempele pali icho. \v 17 Zonse zamene siziliza ulungamo ni chimo, koma kuli chimo yamene siipelekaku imfa.