nya-x-nyanja_1jn_text_reg/04/19.txt

1 line
339 B
Plaintext

\v 19 Timakonda chifukwa mulungu anatikonda pachiyambi. \v 20 Ngati alionse akamba,''Nikonda Mulungu,''koma siakonda mubale wake, niwaboza.koma wamene siakonda mubale wake, wamene siangakonde Mulungu wamene sianaone. \v 21 Ndiponso iyi ndiye lamulo yamene tilinayo kuchekela kwa iye: Wamene akonda Mulungu afunikanso kukonda mubale wake.