nya-x-nyanja_1jn_text_reg/04/01.txt

1 line
442 B
Plaintext

\c 4 \v 1 Okondewa,osakululupira muzimu olionse,koma yesani mizimu zonse kuziba ngati ichokela kuli mulungu,cifukwa aneneli aboza agena muziko. \v 2 Pali ichi muzaziba muzimu wa mulungu-muzimu ulionse wamene uzavomela kuti Yesu Kristu anabwela mu munthu achokela kuli mulungu, \v 3 ndiponso muzimu alionse wamene siuvomela Yesu siuchokela kuli mulungu. Uyu nimuzimu osusana na kristu,wamene munanvela ati ubwela,ndiponso unabwela kudala.