nya-x-nyanja_1jn_text_reg/03/23.txt

1 line
319 B
Plaintext

\v 23 iyi ndiye lamulo lake: Kuti tikulupilile muzina ya mwana wake Yesu Kristu ndi kukondana wina ndi muzake, monga mwamene anati phasila malamulo aya. \v 24 Amene asunga malamulo a Mulungu ankhalilila mwa iye, ndipo Mulungu ankhalilila mwa iye. Mwaichi tiziba kuti akhalilila mwaise, mwa Muzimu wamene iye anatipasa.