nya-x-nyanja_1jn_text_reg/03/13.txt

1 line
302 B
Plaintext

\v 13 Osankhala wodabwa, abale anga, ngati ziko ikuzondani. \v 14 Tiziba kuti tinapita kucoka ku ifa ndikuyenda kumoyo, chifukwa tikonda abale athu. \v 15 Aliyense wamene sakonda akhalila muimfa. Aliyese wamene azonda mbala wake niwakupha. Ndipo muziba ati umoyo wosatha siwu nkhala mu munthu wakupha.