\v 3 Chija camene tinaona ndi kumva ticilankhulanso kwa inu, kuti munkhalenso ndi chiyanjano ndi ife. Chiyanjano cathu cili ndi Atate ndi Mwana, Yesu Kristu. \v 4 Futi tilemba vinthu ivi kuli imwe kuti chimwemwe cathu cinkhale cokwanila.