Fri Nov 09 2018 19:34:58 GMT+0200 (South Africa Standard Time)

This commit is contained in:
tsDesktop 2018-11-09 19:34:58 +02:00
parent f5f83ecf65
commit bec68060c8
5 changed files with 5 additions and 5 deletions

View File

@ -1 +1 @@
\v 4 \v 6 Munachokela kuli mulungu, imwe bana,ndiponso munabagonjeza,cifukwa wamene alimuli iwe niopambana kuchila wamene alimu ziko. \v 5 Bachokela muziko, navamene bamakamba vichokela muziko,naziko imabanvelela. Ise tichokela kuli Mulungu. Wamene aziba Mulungu amatinvelela. Wamene siachokela kuli Mulungu samatinvelela. Pali ichi tizaziba muzimu wachoonadi namu zimu waboza.
\v 4 Munachokela kuli mulungu, imwe bana,ndiponso munabagonjeza,cifukwa wamene alimuli iwe niopambana kuchila wamene alimu ziko. \v 5 Bachokela muziko, navamene bamakamba vichokela muziko,naziko imabanvelela. \v 6 Ise tichokela kuli Mulungu. Wamene aziba Mulungu amatinvelela. Wamene siachokela kuli Mulungu samatinvelela. Pali ichi tizaziba muzimu wachoonadi namu zimu waboza.

View File

@ -1 +1 @@
\v 7 \v 8 Bokondedwa,tiyeni tikondane,cifukwa chikondi chichokela kuli mulungu.Nabonse bana konda nibobadwa kuli mulungu ndiposo bamuziba mulungu. Muntu wamene siamakonda siaziba mulungu,cifukwa mulungu ndiye chikondi.
\v 7 Bokondedwa,tiyeni tikondane,cifukwa chikondi chichokela kuli mulungu.Nabonse bana konda nibobadwa kuli mulungu ndiposo bamuziba mulungu. \v 8 Muntu wamene siamakonda siaziba mulungu,cifukwa mulungu ndiye chikondi.

View File

@ -1 +1 @@
\v 9 \v 10 Cifukwa chaichi chikondi cha mulungu chinavumbulisiwa pali ise,kuti mulungu anatuma mwana wake eka muziko pakuti tinkale cifukwa cha iye. Umu mu chikondi,sikuti tinamukonda mulungu,koma anatikonda,ndiponso anatuma mwana wake kunkala otikambilako kuma chimo watu.
\v 9 Cifukwa chaichi chikondi cha mulungu chinavumbulisiwa pali ise,kuti mulungu anatuma mwana wake eka muziko pakuti tinkale cifukwa cha iye. \v 10 Umu mu chikondi,sikuti tinamukonda mulungu,koma anatikonda,ndiponso anatuma mwana wake kunkala otikambilako kuma chimo watu.

View File

@ -1 +1 @@
\v 11 \v 12 \v 13 \v 14 Bokondedwa,ngati mulungu anatikonda,naise tikondane. Kulibe anaonapo mulungu. Ngati tikondana mulungu ankala muli ise. Nachikondi chake nichosilizika muli ise. Pali ichi tiziba ati tinkalilila muli iye na iye muli ise,chifukwa anatipasako mbali mbali yamuzimu wake. Ndiponso,tinaona ndikupelekela umboni kuti mulungu anatuma mwana wake kubwela kunkala mupulumusi wa ziko.
\v 11 Bokondedwa,ngati mulungu anatikonda,naise tikondane. \v 12 Kulibe anaonapo mulungu. Ngati tikondana mulungu ankala muli ise. Nachikondi chake nichosilizika muli ise. \v 13 Pali ichi tiziba ati tinkalilila muli iye na iye muli ise,chifukwa anatipasako mbali mbali yamuzimu wake. \v 14 Ndiponso,tinaona ndikupelekela umboni kuti mulungu anatuma mwana wake kubwela kunkala mupulumusi wa ziko.

View File

@ -1 +1 @@
\v 15 \v 16 Aliyense wamene azavomela ati Yesu nimwana wa mulungu,mulungu azankala mulu iye. Ndiponso taziba na khukululupira chikondi chamene mulungu alinacho pali ise. Mulungu nichikondi,nawemene ankala muli ichi chikondi ankala muli mulungu,ndiponso mulungu ankala muli iye.
\v 15 Aliyense wamene azavomela ati Yesu nimwana wa mulungu,mulungu azankala mulu iye. \v 16 Ndiponso taziba na khukululupira chikondi chamene mulungu alinacho pali ise. Mulungu nichikondi,nawemene ankala muli ichi chikondi ankala muli mulungu,ndiponso mulungu ankala muli iye.