Fri Nov 09 2018 15:55:49 GMT+0200 (South Africa Standard Time)

This commit is contained in:
tsDesktop 2018-11-09 15:55:49 +02:00
parent 3797680cc9
commit 3308cb45e0
3 changed files with 3 additions and 3 deletions

View File

@ -1 +1 @@
\c 1 \v 1 Icho camene cenzeko kufumila pachiyambi, camene tinamvwa, camene tinaona na menso yasu, chamene tinapenyesesa, camen tinakata ndi manja yathu - ni ca Mau ya moyo. \v 2 Moyo, unazibisidwa, ndipo nauona, ndipo tiucitila umboni. Tikulalikilani kwa inu za umoyo wosatha, wamene unali ndi Atate, ndipo waziwika kuli ife.
\c 1 \v 1 Icho camene cenzeko kufumila pachiyambi, camene tinamvwa, camene tinaona na menso yasu, chamene tinapenyesesa, camen tinakata ndi manja yathu - ni ca Mau ya moyo. \v 2 Moyo, unazibisidwa, ndipo nauona, ndipo tiucitila umboni. Tikulalikilani kwa inu za umoyo wosatha, wamene unali ndi Atate, ndipo waziwika kwa ife.

View File

@ -1 +1 @@
\v 3 Chija camene tinaona ndi kumva ticilankhulanso kwa inu, kuti munkhalenso ndi chiyanjano ndi ife. Chiyanjano cathu cili ndi Atate ndi Mwana, Yesu Klistu. \v 4 Futi tilemba vinthu ivi kuli imwe kuti chimwemwe cathu cinkhale cokwanila.
\v 3 Chija camene tinaona ndi kumva ticilankhulanso kwa inu, kuti munkhalenso ndi chiyanjano ndi ife. Chiyanjano cathu cili ndi Atate ndi Mwana, Yesu Kristu. \v 4 Futi tilemba vinthu ivi kuli imwe kuti chimwemwe cathu cinkhale cokwanila.

View File

@ -1 +1 @@
\v 5 Uyu ndiye Uthenga wamene tinamva, kucokela kwa iye ndi kulalikidwa kwa inu: Mulungu ndiye kuunika, ndipo mwayeve mulibiletu mudima. \v 6 Pamene tikamba kuti tili muciyanjano ndi iye ndipo tuyenda mumdima, tikamba boza ndipo siticita coonadi. \v 7 Koma ngati tiyenda mukuunika mwamene iye ali kuunika, ndipo mlopa wa Yesu mwana wake utisunkha kumachimo athu.
\v 5 Uyu ndiye Uthenga wamene tinamva, kucokela kwa iye ndi kulalikidwa kwa inu: Mulungu ndiye kuunika, ndipo mwayeve mulibiletu mudima. \v 6 Pamene tikamba kuti tili mucigwilizano ndi iye ndipo tuyenda mumdima, tikamba boza ndipo siticita coonadi. \v 7 Koma ngati tiyenda mukuunika mwamene iye ali kuunika, ndipo mlopa wa Yesu mwana wake utisunkha kumachimo athu.