Tue Jul 02 2019 23:15:21 GMT+0200 (South Africa Standard Time)
This commit is contained in:
commit
2465144b81
|
@ -1 +1,5 @@
|
|||
Mutu 1
|
||||
<<<<<<< HEAD
|
||||
Mutu 1
|
||||
=======
|
||||
Mutu Oyamba
|
||||
>>>>>>> f9b85f0fb5d2dca6e2a51fb817caf4e20d339727
|
||||
|
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\c 2 \v 1 Imwe bana bango'no, nikulembelani izi zinthu kuti musachimwe.koma ngati wina achimwa, tilinaye otipapatila ndi atata, Yesu Kristhu wamene ali oyela. \v 2 Ni muombolo wama chimo yatu, Ndiponso siise teka, Ndiponso wa ziko lonse. \v 3 Paliichi tiziba kuti timuziba:ngati tasunga malamulo yake.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 4 Wamene akamba, ''Ati ni muziba Mulungu,'' koma siasunga malamulo yake,ni waboza, na choonadi sichi muli iye. \v 5 koma wamene asunga mau yake,choonadi, ndiye wamane batate ba konda ndi choonadi chake ni chosilizika. paliichi tiziba kuti, timuziba. \v 6 Wamene akamba kuti azankalili muli iye, afunikila kuyenda monga mwame Yesu Kristhu anaendela.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 7 Okondedwa, sinikulembela malamulo ya sopano kuli iwe, koma niya kudala yamene munali nayo pachiyambi. malamulo yakudala ndiye mau unamvela. \v 8 komanso ni kulembela malamulo yasopano kuli iwe, ndiye ya choonadi muli kristhu, chifukwa mfinzi ilikupita, ndi nyali yachendi ilikuwala kudala.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 9 Iye wamene anena kuti ali munyali koma azonda mubale wake akali munfinzi namanje. \v 10 wamene akonda mubale wake ankalilila mu nyali ndiponso kulibe chamene chingamulenge kuzibuntula. \v 11 koma wamene azonda mubale wake alimunfinzi ndiponso akalikuyendela munfinzi; ziazi kwamene ayenda, chifukwa nfinzi yaboola menso yake.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 12 Nilembela imwe, bana, chifukwa machimo yanu yakululukidwa chifukwa chazina yake. Nilembela kwainu azitate, chifukwa muziba wamene ili kuchiyambi. \v 13 Nilembela inu amuna achichepele, chifukwa muna gonjesa woyipa. \v 14 Nalembela kwainu atate, chifukwa mumuziba uja wamene anali kuchiyambi. Nalembela kwainu amuna achichepele, chifukwa ndimwe olimba, ndipo mau ya Mulungu yankalilila mwa imwe. ndiponso mwagonjesa uja woyipa.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 15 Musakonde ziko angankale zinthu zamenezili muziko. ngati wina wache akonda ziko, ndi chikondi chaatate sichili muli iye. \v 16 chifukwa zonse zamene zili muziko__kukumbwila paza muthupi, kukumbwila kwa menso,ndi ntota zaumoyo__siwakuli atate koma niwa kuziko. \v 17 ziko ndizo lakalaka zache zili kupita. koma alionse wamene achita chifunilo cha Mulungu azankalilila muyayaya.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 18 Imwe bana bango'no, iyi ni ntawi yosilizila, monga mwamene munamvelela kuti bambili bosusana kristhu babwela.paichi tiziba kuti ni ntawi yosilizila. \v 19 Banachokela kuliise , koma sibana chokele mwaise. chifukwa ngati banalikuchokela mwaise, asembe anankhalilila mwaise. koma pamene banaenda, sibalangiza kuchokela kuliise.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 20 Koma mulina muzozo kuchokela kuli oyela.ndiponso bonse muziba choonadi. \v 21 sininalembele kwa imwe chifukwa simunazibe choonadi, koma chifukwa muchiziba ichi ndiponso chifukwa kulibe boza yamene ichokela mu choonadi.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 22 Ni ndani waboza koma uja wamene akana Yesu kuti ni Kristhu? uja muntthu ni osusana kristhu, chifukwa akana atate ndi mwana. \v 23 kulibe wamene aka mwana angankale na tate.Alionse wamene azindikila mwana ndiiyenso alinatate.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 24 koma kwaimwe,siyani vamene munasiya kuchiyambi visale muli imwe.ngati vamene munamvela kuchiyambi vasalila mwaimwe, ndiponso muzankhalilila mu mwana ndi atate. \v 25 Iyi ndiye lonjezo anatipasila: moyo wamuyayaya. \v 26 Nalemba izi zinthu kamba kabamene bangakukusobeseni.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 27 Koma kwaiwe, muzozo wamene unalandila kuchoka kuli iye unkhalilile, ndiponso siufunika wina kukupunzisa. koma mwamene muzozo wake umapunzisila imwe zonse ndiponso ni wachoonadi siwaboza,monga mwamene anakuuzilani nkhalililani muli emve. \v 28 Manje,imwe bana, nkhalililani muli iye, pakuti akaonekela, tizankhala olimba muthima ndiponso sitizamvesewa manyazi pakubwela kwake. \v 29 Ngati muziba kuti niolungama, muziba kuti ali onse wamene amachita cholungama niobadwa kuchokela kwaiye.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
MUTU 2
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\c 3 \v 1 Onani chikondi camene Atate anatipasa ife, kuti tiitanidwe ana a Mulungu, ici ndi mwamene tilili. Pa chifukwa ici, dziko lapatsi siitiziba, chifukwa siinamuzibe iye. \v 2 Wokondedwa, manje ndife bana ba Mulungu, ndipo cenze cikalimbe kuonesewa mwamene cizankhalila. Tiziba kuti pamene kristu azaonekela, tizankala ngati iye, chifukwa tizamuona mwemene alili. \v 3 Aliwonse alina chisimikizo cazakusogolo aika nzelu zake mwaiye ndipo aziiyelesa mwamene iye ali woyela.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 4 Aliwonse wamene apitiliza kucimwa achita vosa vomelekezedwa, cimo nicosa vomelekezedwa. \v 5 Muziba kuti Kristu anaonesedwa kuti achose cimo. Ndipo mwa iye mulibe cimo. \v 6 Kulibe amene akhala mwa iye apitiliza kucimwa, kulibe amene apitiliza kuchimwa anamuona kapena kumuziba iye.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 7 Bana anga okondedwa, musalole aliwose akusobeseni. wamene achita chilungamo niolungama. \v 8 Monga Kristu niolungama.Amene acita cimo ni wasatana, Chifukwa satana anacimwa kuchoka pachiyambi. Pa chifukwa ici mwana wa Mulungu anaonesedwa, kuti aononge nchito ya satana
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 9 Aliwonse anabadwa mwa Mulungu samachimwa chifukwa mbeu ya Mulungu inkhalilila mwa iye Sangapitilize kuchimwa chifukwa anabadwa kufumila mwa Mulungu. \v 10 Mwaichi bana ba Mulungu ndi ana ba satana ba onekela. Aliyense wamene sachita chilungamo sachokela kwa Mulungu, ngakale iye amene sakonde mbale wake.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 11 Uyu ndiye uthenga wamene munavela kufumila pachiyambi: kuti tizikondana wina ndi muzake, \v 12 osati monga Kaini, amene anacoka kuwoyipa napaya mubale wake. Nanga anamu paila chani? chifukwa nchito zake zinali zoyipa, ndipo mbale wake zinali zachilungamo.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 13 Osankhala wodabwa, abale anga, ngati ziko ikuzondani. \v 14 Tiziba kuti tinapita kucoka ku ifa ndikuyenda kumoyo, chifukwa tikonda abale athu. \v 15 Aliyense wamene sakonda akhalila muimfa. Aliyese wamene azonda mbala wake niwakupha. Ndipo muziba ati umoyo wosatha siwu nkhala mu munthu wakupha.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 16 Mwaichi tiziba chikondi, chifukwa Kristu anataya moyo wake chifukwa ca ise.naise tifunika kutaya moyo wake chifukwa cha abale athu. \v 17 koma aliyese ali na kathundu wamuziko, naona mbale wake akufuna nakuvala mutima wake wachifundo kwayeve, Nanga chikondi cha Mulungu chinkhala bwaji mwa iye? \v 18 Bana banga okondedwa, tisakonde ndi mau cabe kapena ndililime cabe, koma mukucita ndi mchoonadi.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 19 Ndi mwaici mwamene tiziba kuti tinachokela kuchoonadi, ndipo tisimikiza mitima yasu pamenso pake. \v 20 Ngati mitima yathu itisusa, Mulungu nimukulu kupambana mitima yathu, Ndipo aziba zithu zonse. \v 21 Wokondedwa, ngati mitima yathu siitisusa, tili ndi chisimikizo kwa Mulungu. \v 22 Chilichonse camene timpempa tiza landila kuchokela kwa iye, chifukwa tisunga malamulo ndipo tichita zamene zimukondwelesa iye.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 23 iyi ndiye lamulo lake: Kuti tikulupilile muzina ya mwana wake Yesu Kristu ndi kukondana wina ndi muzake, monga mwamene anati phasila malamulo aya. \v 24 Amene asunga malamulo a Mulungu ankhalilila mwa iye, ndipo Mulungu ankhalilila mwa iye. Mwaichi tiziba kuti akhalilila mwaise, mwa Muzimu wamene iye anatipasa.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
Mutu 3
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\c 4 \v 1 Okondewa,osakululupira muzimu olionse,koma yesani mizimu zonse kuziba ngati ichokela kuli mulungu,cifukwa aneneli aboza agena muziko. \v 2 Pali ichi muzaziba muzimu wa mulungu-muzimu ulionse wamene uzavomela kuti Yesu Kristu anabwela mu munthu achokela kuli mulungu, \v 3 ndiponso muzimu alionse wamene siuvomela Yesu siuchokela kuli mulungu. Uyu nimuzimu osusana na kristu,wamene munanvela ati ubwela,ndiponso unabwela kudala.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 4 Munachokela kuli mulungu, imwe bana,ndiponso munabagonjeza,cifukwa wamene alimuli iwe niopambana kuchila wamene alimu ziko. \v 5 Bachokela muziko, navamene bamakamba vichokela muziko,naziko imabanvelela. \v 6 Ise tichokela kuli Mulungu. Wamene aziba Mulungu amatinvelela. Wamene siachokela kuli Mulungu samatinvelela. Pali ichi tizaziba muzimu wachoonadi namu zimu waboza.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 7 Bokondedwa,tiyeni tikondane,cifukwa chikondi chichokela kuli mulungu.Nabonse bana konda nibobadwa kuli mulungu ndiposo bamuziba mulungu. \v 8 Muntu wamene siamakonda siaziba mulungu,cifukwa mulungu ndiye chikondi.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 9 Cifukwa chaichi chikondi cha mulungu chinavumbulisiwa pali ise,kuti mulungu anatuma mwana wake eka muziko pakuti tinkale cifukwa cha iye. \v 10 Umu mu chikondi,sikuti tinamukonda mulungu,koma anatikonda,ndiponso anatuma mwana wake kunkala otikambilako kuma chimo watu.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 11 Bokondedwa,ngati mulungu anatikonda,naise tikondane. \v 12 Kulibe anaonapo mulungu. Ngati tikondana mulungu ankala muli ise. Nachikondi chake nichosilizika muli ise. \v 13 Pali ichi tiziba ati tinkalilila muli iye na iye muli ise,chifukwa anatipasako mbali mbali yamuzimu wake. \v 14 Ndiponso,tinaona ndikupelekela umboni kuti mulungu anatuma mwana wake kubwela kunkala mupulumusi wa ziko.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 15 Aliyense wamene azavomela ati Yesu nimwana wa mulungu,mulungu azankala mulu iye. \v 16 Ndiponso taziba na khukululupira chikondi chamene mulungu alinacho pali ise. Mulungu nichikondi,nawemene ankala muli ichi chikondi ankala muli mulungu,ndiponso mulungu ankala muli iye.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 17 Chifukwa chaichi,ichi chikondi chankala chosililizika pali ise,pakuti tikankale nachisindikizo pasiku yoweluza, monga mwamene alili,ndiye mwamene tilili muziko. \v 18 Kulibe manta muchikondi.malo mwa,chikondi chosilizika chimataya manta,chifukwa manta iyendelana na chilango. Koma wamene ayopa sanasilizike mu chikondi.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 19 Timakonda chifukwa mulungu anatikonda pachiyambi. \v 20 Ngati alionse akamba,''Nikonda Mulungu,''koma siakonda mubale wake, niwaboza.koma wamene siakonda mubale wake, wamene siangakonde Mulungu wamene sianaone. \v 21 Ndiponso iyi ndiye lamulo yamene tilinayo kuchekela kwa iye: Wamene akonda Mulungu afunikanso kukonda mubale wake.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
Muntu 4
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\c 5 \v 1 Alionse wamene akhulupilila kuti Yesu anabadwa kwa Mulungu, ndiponso wamene akonda tate ndiponso akonda mwana wamene anabadwa kwaiye. \v 2 chifukwa chaichi tiziba kuti tikonda bana bamulungu: ngati takonda ndi kuchita malamulo yamulungu. \v 3 ichi ndiye chikondi chamulungu: kuti tisunge malamulo yake. ndimalamulo yake siyolema.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 4 Aliyense wamene anabadwa kwa Mulungu anagonjesa ZIKO.Ndiponso uku ndiye kupambana kuna gonjesa ziko: mwa chikulupililo chatu. \v 5 Ni ndani wamene angagonjese ziko? Iye wamene akulupilila kuti Yesu ni mwana wa Mulungu.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 6 Uyu ndiye wamene ana choka ku manzi ndi ku mwazi: Yesu Kristhu.Sianabwele chabe na manzi, koma na manzi ndi mwazi. \v 7 koma kuli zitatu zamene zipeleka umboni: \v 8 Muzimu, manzi ndi mwazi. izi zitatu zimavomekezana.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 9 Ngati talandila umboni kuchokela kubanthu, umboni wa mulungu ni wa ukulu. koma umboni wa Mulungu ndiye uyu ,kuti anapeleka umboni wa mwana wake. \v 10 Aliyense wamene akululupila mwana wa Mulungu alina umboni kwa iye eka.aliyense wamene siakululupila Mulungu azipanga eka kumkhala waboza, chifukwa sianakululupile umboni wamene mulungu unapasiwa kamba ka mwana wake.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 11 Ndi umboni ni uyu: Mulungu anatipasa umoyo wamuyayaya, ndi uyu umoyo uli mu mwana wake. \v 12 wamene alina mwana wake alina umoyo.Iye wamene alibe mwana wa Mulungu alibe umoyo.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 13 Nilembela izi zinthu kuti, kuti muzibe kuti mulina umoyo wamuyayaya__kuli imwe bamene bakulupilila mu zina la mwana wa Mulungu. \v 14 Ndiponso ichi ndiye chizindikilo chamene tili nacho mwa iye, kuti tikamufunsa chilichonse kulinganila na chifuniro chake, ama timvela. \v 15 Ndiponso, ngati amatimvela ise_ chilichonse chamene tizamufunsa_tiziba kuti tapasidwa chamene tamufunsa.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 16 Ngati alionse aona mubale wake achita chimo yamene siipeleka kuimfa, afunika apempele, ndi Mulungu azamupasa umoyo. nikamba oaliaboabo bamene machimo yao siapeleka kuimfa. kuli chimo yamene isanduka ku imfa; sinikamba kuti anga pempele pali icho. \v 17 Zonse zamene siziliza ulungamo ni chimo, koma kuli chimo yamene siipelekaku imfa.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 18 Tiziba kuti onse wamene anabadwa kwa Mulungu siamachimwa. koma uyo wamene anabadwa kuchokela kwa Mulungu amamusunga bwino kwaiyo eka, ndiponso uja woipa sianga muononge. \v 19 Tiziba kuti tichokela kwa Mulungu, ndiponso tiziba kuti ziko lonse zinkala muzoipa.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 20 Koma tiziba kuti mwana wamulungu anabwela, ndiponso anatipasa kumvesesa uyo wamene ilina choonadi.koma, tilinaye wamene alina choonadi, mu mwana wake Yesu kristhu.Mulungu ndiye choonadi ndi moyo wamuyayaya. \v 21 Imwe bana, zichosenikoni kumafano.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
MUTU 5
|
|
@ -1 +1,5 @@
|
|||
1 Yohane
|
||||
<<<<<<< HEAD
|
||||
1 Yohane
|
||||
=======
|
||||
Yohane oyamba
|
||||
>>>>>>> f9b85f0fb5d2dca6e2a51fb817caf4e20d339727
|
||||
|
|
|
@ -33,14 +33,57 @@
|
|||
],
|
||||
"parent_draft": {},
|
||||
"translators": [
|
||||
"Abraham Chitambi"
|
||||
"Abraham Chitambi",
|
||||
"febby kabemba",
|
||||
"Dorcas Nkandu",
|
||||
"Sheba Nkandu",
|
||||
"MATHEW_009-PROSPER"
|
||||
],
|
||||
"finished_chunks": [
|
||||
"front-title",
|
||||
"01-title",
|
||||
"01-01",
|
||||
"01-03",
|
||||
"01-05",
|
||||
"01-08"
|
||||
"01-08",
|
||||
"02-title",
|
||||
"02-01",
|
||||
"02-04",
|
||||
"02-07",
|
||||
"02-09",
|
||||
"02-12",
|
||||
"02-15",
|
||||
"02-18",
|
||||
"02-20",
|
||||
"02-22",
|
||||
"02-24",
|
||||
"02-27",
|
||||
"03-title",
|
||||
"03-01",
|
||||
"03-04",
|
||||
"03-07",
|
||||
"03-09",
|
||||
"03-11",
|
||||
"03-13",
|
||||
"03-16",
|
||||
"03-19",
|
||||
"03-23",
|
||||
"04-title",
|
||||
"04-01",
|
||||
"04-04",
|
||||
"04-07",
|
||||
"04-09",
|
||||
"04-11",
|
||||
"04-15",
|
||||
"04-17",
|
||||
"04-19",
|
||||
"05-title",
|
||||
"05-01",
|
||||
"05-04",
|
||||
"05-06",
|
||||
"05-09",
|
||||
"05-11",
|
||||
"05-13",
|
||||
"05-16",
|
||||
"05-18",
|
||||
"05-20"
|
||||
]
|
||||
}
|
Loading…
Reference in New Issue