nya-x-nyanja_1jn_text_reg/02/24.txt

1 line
278 B
Plaintext
Raw Normal View History

\v 24 koma kwaimwe,siyani vamene munasiya kuchiyambi visale muli imwe.ngati vamene munamvela kuchiyambi vasalila mwaimwe, ndiponso muzankhalilila mu mwana ndi atate. \v 25 Iyi ndiye lonjezo anatipasila: moyo wamuyayaya. \v 26 Nalemba izi zinthu kamba kabamene bangakukusobeseni.